Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/13 tsamba 8
  • Ndandanda ya Mlungu wa January 6

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa January 6
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 6, 2014
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 12/13 tsamba 8

Ndandanda ya Mlungu wa January 6

MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 6, 2014

Nyimbo Na. 120 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 6 ndime 1-6 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Genesis 1-5 (Mph. 10)

Na. 1: Genesis 4:1-16 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Anthu Amene Ali M’chipembedzo Choona Amalalikira za Ufumu wa Mulungu Mwakhama—rs tsa. 90 ndime 4 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Mkhristu Ayenera Kuchita Chiyani Akasemphana Maganizo Ndi Mkhristu Mnzake pa Nkhani za Bizinezi?—lv tsa. 222-223 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 125

Mph. 5: Zimene Munganene Pogawira Magazini mu January. Nkhani yokambirana. Kwa masekondi 30 mpaka 60, fotokozani chifukwa chake magaziniwo angakhale othandiza m’gawo lanu. Kenako, pogwiritsa ntchito nkhani zoyambirira za mu Nsanja ya Olonda, pemphani omvera kuti anene funso lochititsa chidwi ndiponso lemba limene angawerenge pogawira magaziniwo. Chitaninso chimodzimodzi ndi nkhani zoyambirira m’magazini ya Galamukani! Ngati nthawi ilipo mungachitenso zimenezi ndi nkhani ina imodzi m’magazini ya Nsanja ya Olonda kapena Galamukani! Chitani chitsanzo chosonyeza mmene mungagawirire magazini iliyonse.

Mph. 10: Zosowa za pampingo.

Mph. 10: Kodi Tikuphunzirapo Chiyani? Nkhani yokambirana. Werengani 1 Akorinto 9:19-23. Kambiranani mmene lemba limeneli lingatithandizire mu utumiki wakumunda.

Nyimbo Na. 7 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena