Ndandanda ya Mlungu wa April 6
MLUNGU WOYAMBIRA APRIL 6
□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:
cl-CN mutu 17, ndime 9-14
□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:
Kuwerenga Baibulo: Eksodo 7-10
Na. 1: Eksodo 9:1-19
Na. 2: Amene Anakhala Ophunzira a Yesu (lr-CN mutu 13)
Na. 3: Kodi Agalatiya 6:2 ndi Agalatiya 6:5 Amatanthauza Chiyani?
□ Msonkhano wa Utumiki:
Mph. 5: Zilengezo.
Mph. 10: Mmene Tingaperekere Zifukwa Zomveka. Nkhani ndi kukambirana ndi omvera, yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, masamba 255-257.
Mph. 20: Achinyamata—Kodi Moyo Wanu Mudzaugwiritsa Ntchito Bwanji? Mkulu akambirane ndi omvera kapepala kakuti Moyo Wanu. Ayamikireni ndi mtima wonse achinyamata obatizidwa amene akuika zinthu za Ufumu patsogolo. Funsani mwachidule mmodzi amene anayamba utumiki wa nthawi zonse ali wachinyamata. M’funseni kuti, ‘Kodi n’chiyani chinakupangitsani kusankha kuchita zimenezi? Kodi mwapeza madalitso otani?’