Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 3/09 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 16

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 16
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 16
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 3/09 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa March 16

MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 16

Nyimbo Na. 106

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 16, ndime 1-11

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Genesis 43-46

Na. 1: Genesis 44: 1-17

Na. 2: Yesu Ali ndi Mphamvu Kuposa Ziwanda (lr-CN mutu 10)

Na. 3: Maulosi a Baibulo Atsimikizira Kukhala Odalirika Kotheratu (rs-CN tsamba 155, ndime 2-5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 130

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Yehova Amadziwika ndi Dzina Lake. Nkhani yokambidwa mwaumoyo yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, patsamba 274, ndime 2-5.

Mph. 10: “Kalata Yochokera ku Bungwe Lolamulira.” Nkhani ndi kukambirana ndi omvera. Ngati nthawi ilipo, pemphani omvera kupereka ndemanga pa malemba omwe ali m’kalatayi.

Mph. 10: N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kusonkhana? Nkhani ndi kukambirana ndi omvera, yochokera mu Nsanja ya Olonda ya May 15, 2007, masamba 11-13. Pemphani omvera kuti afotokoze phindu limene apeza chifukwa chosonkhana komanso zimene amachita kuti azipezeka pamisonkhano mokhazikika ngakhale pali zolepheretsa zina.

Nyimbo Na. 97

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena