Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/13 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 12

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 12
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 12
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 8/13 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa August 12

MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 12

Nyimbo Na. 103 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 27 ndime 10-18 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Aroma 5–8 (Mph. 10)

Na. 1: Aroma 6:21–7:1-12 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: N’chifukwa Chiyani Akhristu Ena Amapita Kumwamba Kukakhala ndi Khristu?—rs tsa. 217 ndime 1-4 (Mph. 5)

Na. 3: N’chifukwa Chiyani Kukonda Kwambiri Zinthu Zakuthupi Kuposa Zinthu Zauzimu Kumabweretsa Mavuto?—Mat. 6:33; 1 Tim. 6:10 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 37

Mph. 10: “Mawu a Mulungu Ndi Opindulitsa pa Kuphunzitsa.” Mafunso ndi mayankho. Lengezani masiku a msonkhano wadera ngati akudziwika.

Mph. 10: Kodi Kukhala ndi Autilaini mu Utumiki N’kothandiza Bwanji? Nkhani yokambirana ndi omvera yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 167 ndime 1 mpaka 168, ndime 1. Pogwiritsa ntchito magazini yogawira mweziwo, sonyezani wofalitsa akulankhula yekha kwa mphindi zingapo pokonzekera zimene akanene mu utumiki.

Mph. 10: Kodi Tikuphunzirapo Chiyani? Nkhani yokambirana. Werengani Machitidwe 8:26-31. Kambiranani mmene malemba amenewa angatithandizire mu utumiki wathu.

Nyimbo Na. 61 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena