Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 7/13 tsamba 8
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 7/13 tsamba 8

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

“Mawu a Mulungu ndi amoyo ndi amphamvu, . . . ndipo amalasa munthu mumtima mpaka kulekanitsa moyo.” (Aheb. 4:12) Mogwirizana ndi mawu amenewa, m’bale wina ali pamalo ake a bizinezi, analalikira Rasi wina. Kuchokera pa nthawi imeneyi, m’baleyu anapitiriza kukambirana ndi munthuyu za m’Baibulo. Kenako anamuitanira ku Nyumba ya Ufumu ndipo anabweradi. Abale anamulandira bwino mosaganizira mmene ankaonekera. Ulendo wotsatira umene munthuyu anabweranso ku Nyumba ya Ufumu, anali atavala bwino komanso atameta tsitsi lake. Tiyeni tipitirize kuthandiza anthu a mitundu yonse kuti adziwe choonadi molondola.—1 Tim. 2:4.

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena