Ndandanda ya Mlungu wa July 27
MLUNGU WOYAMBIRA JULY 27
□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:
cl-CN mutu 23 ndime 1-9
□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:
Kuwerenga Baibulo: Numeri 1-3
Na. 1: Numeri 3:1-20
Na. 2: Chifukwa Chake Kufatsa Kumafuna Kudziletsa
Na. 3: Kodi Mulungu Wanu Ndani? (lr-CN mutu 27)
□ Msonkhano wa Utumiki:
Mph.5: Zilengezo.
Mph.10: Gwiritsani Ntchito Mafunso Mwaluso. Kukambirana ndi omvera kuchokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, masamba 236 mpaka 237 ndime 2. Chitani chitsanzo mwachidule chosonyeza mmene tingagwiritsire ntchito mfundo imodzi kapena ziwiri za m’nkhaniyi.
Mph.10: Funsani makolo awiri kapena atatu a chitsanzo chabwino. Kodi amathana bwanji ndi mavuto amene amakumana nawo pochita utumiki monga banja? Kodi akuchita zotani pofuna kuthandiza ana awo kuti azikonda utumiki? Kodi akuchita zotani pa pulogalamu yawo ya Kulambira kwa Pabanja n’cholinga choti athandize ana awo kukonzekera utumiki?
Mph.10: “Lemekezani Yehova Tsiku Lililonse.” Kambiranani mwa mafunso ndi mayankho.