Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 7/09 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa July 20

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa July 20
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JULY 20
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 7/09 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa July 20

MLUNGU WOYAMBIRA JULY 20

Nyimbo Na. 73

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 22 ndime 15-22 ndi bokosi la patsamba 228

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Levitiko 25-27

Na. 1: Levitiko 25:39-54

Na. 2: Chifukwa Chake Kuchita Zinthu Zabwino Kumavuta (lr-CN mutu 26)

Na. 3: Kodi Adamu Akanapanda Kuchimwa, Akanapita Kumwamba? (rs-CN tsa. 204 ndime 3 ndi 4)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 46

Mph.5: Zilengezo.

Mph.10: Kumanga Pamaziko a Khristu. Nkhani yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, patsamba 278, ndime 1 mpaka 4.

Mph.10: Konzekerani Kugawira Magazini ya Nsanja ya Olonda ya August 1 ndi Galamukani! ya August. Pambuyo pofotokoza mwachidule zimene zili m’magaziniwo, pemphani omvera kuti atchule nkhani zimene akuona kuti zingasangalatse anthu a m’gawolo ndiponso chifukwa chake. Pemphani omvera kuti atchule mafunso amene angafunse poyamba kukambirana ndiponso atchule lemba limene angawerenge asanagawire magaziniyo. Pomaliza, chitani zitsanzo ziwiri zosonyeza mmene tingagawirire magazini iliyonse.

Mph.10: “Kugawira Magazini.” Nkhani yokambirana ndi omvera, ikambidwe ndi woyang’anira utumiki.

Nyimbo Na. 65

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena