Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 3/09 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 9

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 9
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 9
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 3/09 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa March 9

MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 9

Nyimbo Na. 202

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 15, ndime 14-23 ndi bokosi

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Genesis 40-42

Na. 1: Genesis 40:1-15

Na. 2: Tifunika Kukana Ziyeso (lr-CN mutu 9)

Na. 3: Samalani ndi Mzimu Wosafuna Kugonjera

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 41

Mph. 5: Zilengezo. Pemphani wofalitsa mmodzi kapena awiri kuti afotokoze zimene anachita pogawira magazini komanso zotsatira zake.

Mph. 15: Pamene Ena Afunsa Chifukwa. Nkhani ndi kukambirana ndi omvera, yochokera pakamutu kakang’ono patsamba 177 m’buku la Sukulu ya Utumiki. Khalani ndi chitsanzo chosonyeza mmene wofalitsa angayankhire mnzake wakuntchito kapena wakusukulu amene akufunsa za chikhulupiriro chathu. Wofalitsayo ayankhe ndi “mtima wofatsa ndi mwa ulemu waukulu.”—1 Pet. 3:15.

Mph. 15: “Konzekerani Chikumbutso Mokwanira.” Nkhani komanso kukambirana ndi omvera. Fotokozani mwachidule zimene mwakonza kwanuko zokhudza Chikumbutso.

Nyimbo Na. 192

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena