Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w97 12/15 tsamba 31
  • Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1997

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1997
  • Nsanja ya Olonda—1997
  • Timitu
  • ANACHITA CHIFUNIRO CHA YEHOVA
  • BAIBULO
  • MAFUNSO OCHOKERA KWA OŴERENGA
  • MBONI ZA YEHOVA
  • MOYO NDI MIKHALIDWE YACHIKRISTU
  • NKHANI ZA MOYO WA ANTHU
  • NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOSIYANASIYANA
  • OLENGEZA UFUMU AKUSIMBA
  • YEHOVA
  • YESU KRISTU
Nsanja ya Olonda—1997
w97 12/15 tsamba 31

Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1997

Zosonyeza Deti la Kope Lopezekamo Nkhaniyo

ANACHITA CHIFUNIRO CHA YEHOVA

Amtama Yesu Kuti Ndiye Mesiya ndi Mfumu, 3/1

Chikhulupiriro cha Makolo Chifupidwa (makolo a Mose), 5/1

Chitsanzo cha Kudzimana ndi Kukhulupirika (Elisa), 11/1

Kupezera Isake Mkazi, 1/1

Mkazi Wanzeru Apeŵa Tsoka (Abigayeli), 7/1

Tate Yemwe Ali Wokonzeka Kukhululukira (fanizo la mwana woloŵerera), 9/1

BAIBULO

Baibulo la Makarios, 12/15

Buku Lapadera, 6/15

Kodi Mulungu Analiuzira Motani? 6/15

Mmene Baibulo Linadzafikira kwa Ife, 8/15, 9/15, 10/15

MAFUNSO OCHOKERA KWA OŴERENGA

Chilango cha imfa, 6/15

Kodi mamvedwe atsopano a “mbadwo” (Mt 24:34) amakhudza 1914? 6/1

Kodi “mbadwo” (Mt 24:34) umapereka lingaliro lakuti mapeto ali kutali kwambiri? 5/1

Kodi Mboni lerolino zikuchitako ntchito yolekanitsa? 7/1

Kugwiritsira ntchito nsapo ndi ntchofu, 2/1

Malonda​—nchifukwa ninji nkofunika kulemba pangano? 8/1

Otembenuka ‘pachisautso chachikulu’? 2/15

Pedophilia, 2/1

Tetragramatoni ya m’Mateyu wa Shem-Tob? 8/15

Upo wa ajuli, 4/1

MBONI ZA YEHOVA

‘Anagula Choonadi’! (Ghana), 12/15

Brosha Lakuti Mulungu Amafunanji, 1/15

Chilakiko ku Greece, 2/1

Chizunzo cha Anazi, 8/15

Khoti Yapamwamba ya ku Connecticut Ichirikiza Zoyenera za Odwala, 8/1

Kodi Nchifukwa Ninji Onse Ayenera Kutamanda Mulungu? (zokumana nazo), 1/1

Kuchezera Munda Wakwathu Waumishonale (C. Seymour), 6/15

Kukonda Osoŵa, 10/1

Kutsiriza Maphunziro a Gileadi, 6/1, 12/1

Kutsutsa Zinenezo ku France, 3/15

Kuwamasula Mwauzimu Andende (Mexico), 2/15

Misonkhano Yachigawo ya “Amithenga a Mtendere Waumulungu,” 1/15

Misonkhano ya Mitundu Yonse, 4/1

“Mmodzi mwa Anthu Ambiri Amene Munakhudza Mtima,” 3/1

Mwambo Wakuchiritsa ndi Opaleshoni Yopanda Mwazi, 2/15

Onga Nkhosa mu Dziko la Anavajo, 8/15

Uthenga Wabwino wa Paradaiso ku Tahiti, 10/15

Zopereka, 11/1

MOYO NDI MIKHALIDWE YACHIKRISTU

Chenjerani ndi “Aepikureya,” 11/1

Chenjerani ndi Kukayikira Zolinga za Ena, 5/15

Chikumbumtima, 8/1

Chiyembekezo Mutataya Mtima, 5/15

Kodi Kudandaula Konse Nkoipa? 12/1

Kodi Mukulakalaka Kuwonjezera Utumiki Wanu? 3/15

Kodi Mumadya Bwino Mwauzimu? 4/15

Kodi Mzimu wa Dziko Ukukuipitsani? 10/1

Kodi Ndinu Bwenzi la Mulungu?​—Mapemphero Avumbula, 7/1

Kufooka kwa Anthu Kusonyeza Mphamvu ya Yehova, 6/1

Kukhulupirika, 5/1

Kulemekeza Makolo Okalamba, 9/1

Kuona Mtima​—Mwamwaŵi Kapena Mosankha? 5/15

Kuopa Kukhulupirira Ena? 3/1

Kuzindikira Pulinsipulo, 10/15

“Lemekeza Yehova ndi Chuma Chako”​—Motani? 11/1

Maukwati Olemekeza Yehova, 4/15

Nkuululiranji Choipa? 8/15

Phunziro la Banja, 8/1

Pulumutsani Moyo wa Mwana Wanu! 7/15

Sungani Chimwemwe mu Utumiki wa Nthaŵi Zonse, 9/15

Tidane Nacho Choipa, 1/1

NKHANI ZA MOYO WA ANTHU

Chidaliro Changa mwa Yehova Chinandichirikiza (A. Paixão), 2/1

Choonadi cha Baibulo Ndinachiphunzirira ku Romania (G. Romocean), 4/1

Kudikirabe Yehova Moleza Mtima Kuyambira Ubwana Wanga (R. Graichen), 8/1

Kulepa Zochuluka Chifukwa cha Kanthu Kena Kokulirapo (J. Owo Bello), 1/1

Mapindu a Utumiki Wopatulika (H. Bloor), 12/1

“M’Malo mwa Golidi, Ndinapeza Madiamondi” (M. Kaminaris), 3/1

Moyo Umene Sindinadandaulepo Nawo (P. Obrist), 7/1

Mtima Wanga Wadzaza Chiyamiko Chosaneneka (J. Wynn), 9/1

Mulungu Ndiye Pothaŵira Panga ndi Mphamvu Yanga (C. Müller), 5/1

Ndinaona “Wamng’ono” Akusanduka “Mtundu Wamphamvu” (W. Dingman), 11/1

Woyamikira Chifukwa Chotumikira Yehova Nthaŵi Yaitali (O. Mydland), 10/1

Yehova Amachita Mokhulupirika (P. Palliser), 6/1

NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRA

“Adalenga Iwo Mwamuna ndi Mkazi,” 6/15

Akristu ndi Dziko la Anthu, 11/1

“Amene Mungakhale Simunamuona Mumkonda,” 2/1

Amithenga a Mtendere Waumulungu Atchedwa Achimwemwe, 5/1

Chenjerani ndi Aphunzitsi Onama! 9/1

Chikhulupiriro Chimatipanga Kukhala Oleza Mtima ndi Olimbikira Kupemphera, 11/15

Chikhulupiriro Chimatisonkhezera Kuchitapo Kanthu! 11/15

Chikondi Chanu cha pa Abale Chikhalebe! 8/1

Chinsinsi Chimene Akristu Sayenera Kusunga! 6/1

“Choyenera Anthu Onse,” 2/15

Funafunani Mtendere Weniweni ndi Kuulondola! 4/15

Gwiritsitsani Chikhulupiriro Chanu Mosasamala Kanthu za Ziyeso! 11/15

Kodi Mudzakhulupirika Monga Eliya? 9/15

Kodi Mukulondola Khalidwe Labwino? 7/15

Kodi Mulungu Amafunanji kwa Ife? 1/15

Kodi Mwakonzekera Tsiku la Yehova? 3/1

Kodi Tikhalire Moyo Zalero Kapena Zamtsogolo Mosatha? 8/15

Kodi Ndani Adzapulumuka “Tsiku la Yehova”? 9/15

Kuchirikiza Mokhulupirika Mawu a Mulungu Ouziridwa, 10/1

Kudziŵa Mtundu Wabwino wa Mthenga, 5/1

Kukhala “Anzeru” Pamene Mapeto Ayandikira, 8/15

Kukhala m’Dziko Koma Osakhala Mbali Yake, 11/1

Kulanditsidwa ndi Kuloŵa m’Dziko Latsopano Lolungama, 4/1

Kumbukirani Tsiku la Yehova Nthaŵi Zonse, 9/1

Kupulumuka ‘Tsiku la Yehova,’ 12/15

Kusunga Khalidwe Labwino m’Dziko Lodzala ndi Makhalidwe Oipa, 7/15

Kuthandiza Ena Kuphunzira Zimene Mulungu Amafuna, 1/15

Kutumikira Limodzi ndi Gulu la Yehova Mokhulupirika, 8/1

Kutumikira Monga Amithenga a Mtendere Waumulungu, 1/15

Kuzindikira Kukuchinjirizeni, 3/15

Limbani Mtima Pamene Chilanditso Chikuyandikira, 4/1

Londolani Mtendere Waumulungu m’Moyo wa Banja, 6/15

Lozetsani Mtima Wanu ku Kuzindikira, 3/15

Madalitso a Utumiki Waupainiya, 10/15

Mawu a Mulungu Akhala Kosatha, 10/1

Moyo Wanu​—Kodi Chifuno Chake Nchiyani? 2/15

Mtendere Weniweni​—Kodi Udzachokera Kuti? 4/15

“Mulungu Anatikonda Ife Kotero,” 2/1

Odala Iwo Amene Adikira! 3/1

Onse Alemekeze Yehova! 1/1

Opatulidwa Kukhala Atamandi Achimwemwe pa Dziko Lonse, 7/1

Palibe Mtendere kwa Amithenga Onyenga! 5/1

Pamene Yesu Afika mu Ulemerero wa Ufumu, 5/15

Perekani Chilengezo Chapoyera cha Chipulumutso, 12/15

‘Pitirizani Kukhululukirana Eni Okha,’ 12/1

Tigwiritse Chikhulupiriro Chathu Chamtengo Wapatali! 9/1

Ulemerero Waukulu Kwambiri wa Nyumba ya Yehova, 1/1

Uyang’aniro Wateokrase m’Nthaŵi ya Akristu, 5/15

Yehova Amayamikira Utumiki Wanu wa Mtima Wonse, 10/15

Yehova, Mulungu “Wokhululukira,” 12/1

Yehova​—Mulungu Wovumbula Zinsinsi, 6/1

“Yehova Sadzasiya Anthu Ake,” 7/1

NKHANI ZOSIYANASIYANA

Achinyamata​—Tsogolo Labwino? 12/1

Akatswiri Odumphadumpha m’Miyala ya m’Mapiri, 7/15

Aristarko, 9/15

Aumphaŵi Komabe Olemera, 9/15

Chimwemwe​—Kodi Mfungulo Yake Nchiyani? 10/15

Chipulumutso, 8/15

Ehudi, 3/15

Enoke, 1/15

Epafra, 5/15

“Kachisi wa Mulungu” ndi Mafano m’Greece, 2/15

Kodi Chikhulupiriro Chimalira Chozizwitsa? 3/15

Kodi Chimwemwe Chingapezeke Kuti? 3/15

Kodi Madyerero a Kututa Amakondweretsa Mulungu? 9/15

Kodi Ozunzika Adzakhaladi ndi Mtendere? 4/15

Krisimasi, 12/15

Kubadwanso m’Moyo Wina, 5/15

Kuchiritsa, 7/1

Kufunitsitsa Dziko Lolungama? 11/15

Kukhalabe Namwali Muukwati? (Mariya), 10/15

Kukhulupirika m’Dziko Lopanda Ungwiro, 5/1

Kuumirira Mwambo, 3/1

“Kuweruza mwa Kufufuza”​—Kodi Nchiphunzitso cha Baibulo? 7/15

Magulu Achinsinsi, 6/1

Malamulo Khumi, 12/1

“Malaya Opatulika a ku Trier,” 4/1

Malo a Nyimbo Pakulambira Kwamakono, 2/1

Masiku Otsiriza, 4/1

Mishnah, 11/15

Naḥmanides​—Kodi Anatsutsa Chikristu? 4/15

Onesiforo, 11/15

Pamene Mavuto Sadzakhalakonso, 2/15

Sekemu​—Mzinda wa m’Chigwa, 2/1

Sukulu Zaboding’i, 3/15

Sunemu​—Wodziŵika ndi Chikondi ndi Chiwawa, 10/1

Tertio, 7/15

Uchimo, 7/15

Ufulu wa Chipembedzo, 2/1

Ukwati wa Zaka 403 Uli m’Vuto (Tchalitchi cha Sweden), 4/1

Umodzi wa Dziko Lonse, 11/1

Yerusalemu m’Nthaŵi za Baibulo, 6/15

Zozizwitsa Zokha Sizimabala Chikhulupiriro, 3/15

OLENGEZA UFUMU AKUSIMBA

2/1, 3/1, 4/1, 6/1, 7/1, 8/1, 9/1, 10/1, 12/1

YEHOVA

Amalamulira Mwachifundo, 12/15

“Mulungu wa Mtendere” Amawasamala Amene Akuzunzika, 4/15

Mulungu wa Umunthu Wake, 10/1

YESU KRISTU

Amtama Kuti Ndiye Mesiya ndi Mfumu, 3/1

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena