Mutu wa Buku Lino/Tsamba la Ofalitsa
Mapeto Osangalatsa a Masomphenya a M’buku la Chivumbulutso Ayandikira
BUKULI NDI LA ․․․․․․․․․․․․․․․․
Losindikizidwa mu 2011
Bukuli sitigulitsa. Timalipereka ngati njira imodzi yophunzitsa anthu Baibulo padziko lonse ndipo ndalama zoyendetsera ntchitoyi ndi zimene anthu amapereka mwa kufuna kwawo.
Malemba onse m’buku lino akuchokera m’Baibulo lolembedwa m’Chichewa chamakono la Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika, kupatulapo ngati tasonyeza Baibulo lina
Mawu a Zithunzi
Pictures are listed by page number and, when necessary, in order of appearance on page (clockwise from top left).
Cooper-Hewitt Museum; drawing based on photo of case 9, panel A: Page 59
National Aeronautics and Space Administration, Washington, D.C.: Pages 138, 293
Pictorial Archive (Near Eastern History) Est.: Page 23 (background, 1, 4, 10)
Pictorial Archive (Near Eastern History) Est., and Survey of Israel; based on a map copyrighted by: Page 236
Staatliche Museen zu Berlin; used with the kind permission of: Page 43 (1, 2, 3)
‘Wodala ndi munthu amene amawerenga mokweza, ndiponso anthu amene akumva mawu a ulosi umenewu, komanso amene akusunga zolembedwamo, pakuti nthawi yoikidwiratu ili pafupi.’—Chivumbulutso 1:3