Zamkatimu
Tsamba Masomphenya Mutu
6 1 Mapeto Osangalatsa a Masomphenya a M’buku la Chivumbulutso
9 2 Mfundo Yaikulu ya M’Baibulo
15 3 Zinthu Zimene Ziyenera Kuchitika Posachedwapa
18 4 Yesu Anabwera ndi Uthenga Wolimbikitsa
22 1 5 Yohane Anaona Yesu Ali mu Ulemerero Wake
27 1 6 Kuulula Chinsinsi Chopatulika
33 1 7 Yambaninso Kukonda Mulungu Ngati Poyamba
37 1 8 Tiyesetse Kuti Tipambane pa Nkhondo
41 1 9 Gwiranibe Mwamphamvu Dzina la Yesu
47 1 10 Muzinyansidwa ndi “Zinthu Zozama za Satana”
54 1 11 Kodi Dzina Lanu Lili M’buku la Moyo?
58 1 12 “Gwirabe Mwamphamvu Chimene Uli Nacho”
66 1 13 Ugule Golide Woyengedwa ndi Moto
74 2 14 Ulemerero wa Mpando Wachifumu wa Yehova Wakumwamba
82 2 15 ‘Ndani Ali Woyenera Kutsegula Mpukutu?’
89 3 16 Anthu Anayi Okwera Mahatchi Ali pa Liwiro
100 3 17 “Miyoyo ya Amene Anaphedwa” Idzalandira Mphoto
104 3 18 Zivomezi za M’tsiku la Ambuye
113 4 19 Kudinda Chidindo Isiraeli wa Mulungu
119 4 20 Khamu Lalikulu Kwambiri
129 5 21 Miliri ya Yehova pa Matchalitchi Achikhristu
142 5 22 Tsoka Loyamba Linali Dzombe
148 5 23 Tsoka Lachiwiri Linali Makamu a Asilikali Okwera Pamahatchi
155 6 24 Uthenga Wozuna Komanso Wowawa
161 6 25 Mboni Ziwiri Zinaukitsidwa
171 6 26 Mapeto Osangalatsa a Chinsinsi Chopatulika cha Mulungu
177 7 27 Ufumu wa Mulungu Wabadwa
186 8 28 Kulimbana ndi Zilombo Ziwiri Zoopsa
198 9 29 Kuimba Nyimbo Yatsopano Yokondwerera Kupambana
205 9 30 “Babulo Wamkulu Wagwa”
215 10 31 Ntchito za Yehova N’zazikulu ndi Zodabwitsa
221 10 32 Kumalizitsa Mkwiyo wa Mulungu
235 11 33 Kuweruza Hule la Makhalidwe Oipa
246 11 34 Chinsinsi Chochititsa Mantha Chinaululika
251 11 35 Kupha Babulo Wamkulu
258 12 36 Mzinda Waukulu Udzawonongedwa
267 12 37 Babulo Akadzawonongedwa, Ena Adzalira Koma Ena Adzasangalala
272 12 38 Tamandani Ya Chifukwa cha Ziweruzo Zake
279 13 39 Mfumu Yankhondo Idzapambana pa Aramagedo
286 14 40 Mutu wa Njoka Udzaphwanyidwa
295 15 41 Tsiku Lopereka Chiweruzo la Mulungu Lidzabweretsa Madalitso Osangalatsa Kwambiri
301 15 42 Kumwamba Kwatsopano ndi Dziko Lapansi Latsopano
305 16 43 Mzinda Wokongola Kwambiri
314 44 Mmene Masomphenya a M’buku la Chivumbulutso Akukukhudzirani
Buku lonse la m’Baibulo la Chivumbulutso lafotokozedwa m’buku lino. Mavesi amene akufotokozedwa alembedwandi zilembo zakuda kwambiri.