Ndandanda ya Mlungu wa August 3
MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 3
Nyimbo Na. 48 ndi Pemphero
Phunziro la Baibulo la Mpingo:
cl mutu 16 ndime 18-22 ndi bokosi patsamba 167 (30 min.)
Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:
Kuwerenga Baibulo: 1 Mafumu 18-20 (8 min.)
Na. 1: 1 Mafumu 18:30-40 (Osapitirira 3 min.)
Na. 2: Akazi Okhulupirira Amatamanda Yehova—bt bokosi tsa. 132 (5 min.)
Na. 3: Kodi Baibulo Lingathandize Bwanji Ana?—igw tsa. 27 ndime 1-2 (5 min.)
Msonkhano wa Utumiki:
Mutu wa Mwezi Uno: ‘Pitani mukaphunzitse anthu kuti akhale ophunzira anga.’—Mat. 28:19, 20.
10 min: Zimene Munganene Pogawira Magazini a August. Nkhani yokambirana. Yambani ndi kuchita zitsanzo zosonyeza zimene tinganene pogawira magaziniwa, pogwiritsa ntchito zitsanzo zaulaliki zomwe zili patsamba lino. Kenako kambiranani chitsanzo cha ulaliki chilichonse kuyambira poyambirira mpaka pamapeto.
10 min: Muzigwiritsa Ntchito Kabuku Kakuti, Kuphunzira Malemba Tsiku ndi Tsiku. Nkhani yokambirana. Yambani ndi kukamba nkhani ya 5 minitsi yochokera pa lemba la chaka cha 2015. Kenako pemphani omvera kuti anene nthawi imene amapanga lemba la tsiku. Pomaliza limbikitsani onse kuti tsiku lililonse azichita lemba la tsiku pogwiritsa ntchito kabukuka.
10 min: Zofunika pampingo.
Nyimbo Na. 26 ndi Pemphero