Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/15 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 18

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 18
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MAY 18
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 5/15 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa May 18

MLUNGU WOYAMBIRA MAY 18

Nyimbo Na. 105 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 13 ndime 1-10 (30 min.)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Samueli 9-12 (8 min.)

Na. 1: 2 Samueli 10:13–11:4 (Osapitirira 3 min.)

Na. 2: Tizilemekeza Akulu Mumpingo—bt tsa. 98-99 ndime 17-20 (5 min.)

Na. 3: Kodi Akufa Adzakhalanso ndi Moyo?—igw tsa. 19 ndime 1-3 (5 min.)

Msonkhano wa Utumiki:

Mutu wa Mwezi Uno: Muzithandiza anthu onse kudziwa choonadi molondola.—1 Tim. 2:3, 4.

Nyimbo Na. 73

10 min: Kodi Paulo Anathandiza Bwanji Agiriki Kudziwa Choonadi Molondola? Nkhani yokambirana. Werengani Machitidwe 17:22-31. Kenako kambiranani mmene mavesi amenewa angatithandizire mu utumiki.

20 min: Yehova Akuthandiza Kuti Ukhale Wolimba Mtima. Nkhani yokambirana. Ikani vidiyo yakuti, Yehova Akuthandiza Kuti Ukhale Wolimba Mtima. (Vidiyoyi ikupezeka pa webusaiti yathu ya jw.org/ny. Pitani pamene palembedwa kuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > ANA.) Pemphani omvera kuti afotokoze zimene tikuphunzira m’vidiyoyi. Pemphaninso ana omwe amapita kusukulu kuti afotokoze mmene vidiyoyi ingawathandizire kuti azikhala olimba mtima akamalalikira anzawo a kusukulu komanso aphunzitsi. Konzani zoti mwana mmodzi achite chitsanzo chosonyeza zosangalatsa zomwe zinachitika pamene ankalalikira kusukulu. Ngati n’zosatheka kuonera vidiyoyi, kambiranani nkhaniyi pogwiritsa ntchito lemba la 2 Mafumu 5:1-19. Pemphani omvera kuti afotokoze zimene tikuphunzira pamavesi amenewa. Pemphaninso ana omwe amapita kusukulu kuti afotokoze mmene nkhaniyi ingawathandizire kuti azilalikira anzawo a kusukulu komanso aphunzitsi molimba mtima. Konzani zoti mwana mmodzi achite chitsanzo chosonyeza zosangalatsa zomwe zinachitika pamene ankalalikira kusukulu.

Nyimbo Na. 60 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena