Ndandanda ya Mlungu wa May 11
MLUNGU WOYAMBIRA MAY 11
Nyimbo Na. 133 ndi Pemphero
Phunziro la Baibulo la Mpingo:
cl mutu 12 ndime 16-21 ndi bokosi patsamba 127 (30 min.)
Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:
Kuwerenga Baibulo: 2 Samueli 4-8 (8 min.)
Na. 1: 2 Samueli 6:14-23 (Osapitirira 3 min.)
Na. 2: Kodi Chimachitika N’chiyani Munthu Akamwalira?—igw tsa. 18 ndime 1-3 (5 min.)
Na. 3: Khalani Odzichepetsa Kuti Musakumane ndi Tsoka Ngati Belisazara—dp tsa. 110 ndime 23-24 (5 min.)
Msonkhano wa Utumiki:
Mutu wa Mwezi Uno: Muzithandiza anthu onse kudziwa choonadi molondola.—1 Tim. 2:3, 4.
10 min: Muzithandiza Anthu Onse Kudziwa Choonadi Molondola. Nkhani yochokera pa mutu wa mwezi uno. (Onani Nsanja ya Olonda ya November 15, 2013, tsa. 11-12 ndime 8.) Werengani ndi kukambirana lemba la 1 Timoteyo 2:3, 4 komanso 1 Akorinto 9:19-23. Tchulani nkhani zomwe tiphunzire mu Msonkhano wa Utumiki mwezi uno ndipo fotokozani kugwirizana kwa nkhanizo ndi mutu wa mwezi uno.
20 min: “Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki—Muzilalikira Anthu Oyankhula Chinenero China.” Nkhani yokambirana. Chitani chitsanzo chachidule chosonyeza wofalitsa akugwiritsa ntchito kabuku ka Uthenga Wabwino wa Anthu a Mitundu Yonse polalikira munthu wachinenero china yemwe wakumana naye pamene amalalikira kunyumba ndi nyumba.
Nyimbo Na. 105 ndi Pemphero