Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/14 tsamba 8
  • Ndandanda ya Mlungu wa January 5

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa January 5
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 5, 2015
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 12/14 tsamba 8

Ndandanda ya Mlungu wa January 5

MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 5, 2015

Nyimbo Na. 33 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 6 ndime 16-21 ndi bokosi patsamba 65 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Yoswa 16-20 (Mph. 8)

Na. 1: Yoswa 17:11-18 (Osapitirira mph. 3)

Na. 2: Kodi Mulungu Ndi Ndani?—igw tsa. 2 ndime 1-3 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Tiyenera Kupewa Chiyani Ngati Zikutiyendera Bwino mu Utumiki?—bt tsa. 29-31 ndime 5-8 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

Mutu wa Mwezi Uno: Tizipereka zinthu “zabwino” zochokera m’chuma chomwe tinapatsidwa.—Mat. 12:35a.

Nyimbo Na. 28

Mph. 30: “Nyimbo Zatsopano.” Onani tsamba 7. Nkhani yokambirana. Mukamakambirana ndime 6, ikani nyimbo yatsopano ya mutu wakuti, “Ufumu Umene Ukulamulira Kumwamba Ubwere.” Pemphani omvera kuti aimirire ndi kuimba nyimboyi. Mungaimbe nyimboyi kawiri kuti anthu aizolowere. Ngati simungathe kupita pa webusaiti ya jw.org kuti muchite dawunilodi nyimboyi, muimbe nyimbo nambala 108 yakuti, “Tamandani Yehova Chifukwa cha Ufumu Wake.”

Nyimbo yatsopano ya mutu wakuti, “Ufumu Umene Ukulamulira Kumwamba Ubwere” ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena