Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 7/14 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa July 21

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa July 21
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JULY 21
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 7/14 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa July 21

MLUNGU WOYAMBIRA JULY 21

Nyimbo Na. 62 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 14 ndime 1-7 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Levitiko 25-27 (Mph. 10)

Na. 1: Levitiko 26:1-17 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Anthu Onse Potsirizira Pake Adzapulumutsidwa?—rs tsa. 95 ndime 1 (Mph. 5)

Na. 3: Mmene Malemba Amasiyanitsira Ngozi Yeniyeni Ndi Zinthu Zadala—lv tsa. 84 ndime 23-25 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 67

Mph. 10: Amatilemekeza Chifukwa cha Khalidwe Lathu Labwino Komanso Chifukwa Chosalowerera Ndale. Nkhani yokambirana yochokera mu Buku Lapachaka la 2014, tsamba 120 ndi 149. Pemphani omvera kuti afotokoze zimene tikuphunzirapo.

Mph. 10: Kodi Mungadzachite Upainiya Wothandiza mu August? Nkhani. Funsani ofalitsa awiri kapena atatu amene akonza zodzachita upainiya m’mwezi wa August ngakhale kuti amadwaladwala kapena amatanganidwa. Kodi adzatani kuti akwanitse kuchita upainiya? Funsani woyang’anira utumiki kuti anene zokhudza misonkhano yokonzekera utumiki m’mwezi wa August.

Mph. 10: “Kodi Yehova Amandiona Kuti Ndine Munthu Wotani?” Mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 65 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena