Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/14 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 26

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 26
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MAY 26
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 5/14 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa May 26

MLUNGU WOYAMBIRA MAY 26

Nyimbo Na. 48 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 12 ndime 1-7 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Ekisodo 34-37 (Mph. 10)

Na. 1: Ekisodo 34:1-16 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Chifukwa Chimene Malamulo Onse Amakhalidwe Abwino Sanachotsedwe Pamene Malamulo Khumi Anachotsedwa—rs tsa. 349 ndime 1-2 (Mph. 5)

Na. 3: N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kuphunzitsa Chikumbumtima Chathu?—lv tsa. 17-19 ndime 8-11 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 32

Mph. 10: Yambitsani Phunziro la Baibulo Loweruka Loyambirira. Nkhani yokambirana. Pemphani omvera kuti afotokoze zinthu zosangalatsa zimene anakumana nazo pamene ankayambitsa maphunziro a Baibulo Loweruka loyambirira la mwezi uno. Pogwiritsa ntchito chitsanzo cha ulaliki chomwe chili patsamba 4, chitani chitsanzo chachidule cha mmene tingayambitsire maphunziro. Limbikitsani onse kuti adzayambitse nawo maphunziro a Baibulo.

Mph. 10: Kupirira Pozunzidwa Kumakhala Ndi Zotsatira Zabwino. (Luka 21:12, 13) Nkhani yokambirana yochokera mu Buku Lapachaka la 2013 tsamba 124 ndime 1 komanso tsamba 128 ndime 1-2. Pemphani omvera kuti afotokoze zimene tikuphunzirapo.

Mph. 10: Bokosi la Mafunso. Nkhani yokambirana yokambidwa ndi mkulu. Pemphani ofalitsa, koma osati ana, kuti afotokoze mmene anapindulira chifukwa chophunzitsidwa mfundo zozama za m’Baibulo ndi makolo awo.

Nyimbo Na. 88 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena