Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/14 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 12

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 12
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MAY 12
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 5/14 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa May 12

MLUNGU WOYAMBIRA MAY 12

Nyimbo Na. 69 ndi Pemphero

jr mutu 11 ndime 9-14 (Mph. 30)

Kuwerenga Baibulo: Ekisodo 27-29 (Mph. 10)

Na. 1: Ekisodo 29:19-30 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Yesu Sanagawe Chilamulo cha Mose Kukhala ndi Mbali ya “Mwambo” ndi ya “Makhalidwe Abwino”—rs tsa. 347 ndime 3–tsa. 348 ndime 1 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Tingatani Kuti Tisiye Kugwirizana ndi Mizimu Yoipa?—bh tsa. 103-104 ndime 14-16 (Mph. 5)

Nyimbo Na. 75

Mph. 15: Mitundu Yonse Idzakhamukira Kumeneko. (Yes. 2:2) Funsani ofalitsa awiri. Mmodzi akhale woti wakhala m’choonadi kwa zaka zambiri ndipo wina akhale woti wangobatizidwa chakumene. Kodi n’chiyani chinawapangitsa kuti aphunzire choonadi? Ndi mavuto ati amene anakumana nawo? Nanga n’chiyani chinawachititsa chidwi pa nthawi yoyamba imene anafika pamisonkhano ya mpingo? Ndi zinthu ziti zimene amakumbukirabe zomwe zinachitika pa tsiku loyamba limene analowa mu utumiki? Kodi abale ndi alongo anawathandiza bwanji kuti apitirizebe kukula mwauzimu?

Mph. 15: “Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki—Muzikonzekera Mawu Oyamba.” Nkhani yokambirana. Chitani chitsanzo cha mbali ziwiri. Mbali yoyamba isonyeze munthu akunena mawu oyamba osonyeza kuti sanakonzekere. Mbali yachiwiri ikhale ndi mawu oyamba osonyeza kuti anakonzekera. Ngati nthawi ilipo, fotokozani mfundo zothandiza pa nkhaniyi zimene zili m’buku la Sukulu ya Utumiki, patsamba 215 mpaka 219.

Nyimbo Na. 117 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena