Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/13 tsamba 7
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 30

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 30
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 30
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 12/13 tsamba 7

Ndandanda ya Mlungu wa December 30

MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 30

Nyimbo Na. 52 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 5 ndime 13-18 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Chivumbulutso 15–22 (Mph. 10)

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu (Mph. 20)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 43

Mph. 10: “Athandizeni Kuti ‘Akhazikike M’chikhulupiriro.’” Nkhani. Pomaliza, chitani chitsanzo chachidule chosonyeza mmene tingayambitsire phunziro la Baibulo Loweruka loyambirira m’mwezi wa January. Limbikitsani onse kuti adzayambitse nawo maphunziro a Baibulo.

Mph. 10: Thandizani Ana Anu Aang’ono Kukhala Ofalitsa. Nkhani yochokera m’buku la Gulu patsamba 81 ndime 4 mpaka tsamba 82 ndime 1. Funsani kholo lachitsanzo chabwino lomwe lili ndi mwana amene ndi wofalitsa wosabatizidwa. Kodi linamuthandiza bwanji kukhala wofalitsa wosabatizidwa?

Mph. 10: Sitikhala Tokha mu Utumiki. (2 Maf. 6:16) Nkhani yokambirana yochokera mu Buku Lapachaka la 2013 tsamba 47 ndime 3 mpaka tsamba 48 ndime 2. Pemphani omvera kuti afotokoze zimene tikuphunzirapo.

Nyimbo Na. 119 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena