Ndandanda ya Mlungu wa December 6
MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 6
□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:
□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:
Kuwerenga Baibulo: 2 Mbiri 10-14
Na. 1: 2 Mbiri 13:1-12
Na. 2: Kodi Yehova Amateteza Motani Atumiki Ake Okondedwa Kapena Kuti Okhulupirika? (Sal. 37:28)
Na. 3: **Ngati Wina Anena Kuti: “N’chifukwa Chiyani Simuchita Nawo Zinthu Zothandiza Kuti Dzikoli Likhale Labwino Kwambiri?” (rs tsa. 278 ndime 4–tsa. 279 ndime 3)
□ Msonkhano wa Utumiki:
Mph. 10: Zilengezo. Pemphani omvera kuti afotokoze zokumana nazo pogawira kapena kuyambitsa maphunziro a Baibulo pogwiritsa ntchito kabuku kakuti Kodi Baibulo Lili Ndi Uthenga Wotani?
Mph. 10: Zosowa za pampingo.
Mph. 15: Mmene Mungalemekezere Ena mu Utumiki. Nkhani yokambirana ndi omvera yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 190 mpaka 192, ndime 2.