Ndandanda ya Mlungu wa October 18
MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 18
□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:
lv mutu 13 ndime 15-25 ndi bokosi patsamba 156a
□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:
Kuwerenga Baibulo: 1 Mbiri 8-11
Na. 1: 1 Mbiri 11:1-14
Na. 2: Kodi Mzimu ndi Mkwatibwi Amanena Kuti, “Bwera,” M’njira Ziti? (Chiv. 22:17)
Na. 3: Kodi Mboni za Yehova Zimakhulupirira Kuti Chipembedzo Chawo Ndicho Chokha Cholondola? (rs tsa. 275 ndime 1 ndi 2)
□ Msonkhano wa Utumiki:
Mph. 5: Zilengezo.
Mph. 10: Chifukwa Chake Kuyang’ana Omvera mu Utumiki N’kofunika. Nkhani yokambirana ndi omvera yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 124, ndime 1, mpaka tsamba 125, ndime 4.
Mph. 20: “Kabuku Katsopano Kamene Tidzagawira.” Nkhani ya mafunso ndi mayankho. Pokambirana ndime 1, fotokozani mwachidule zimene zili m’kabukuka. Mukamaliza kukambirana ndime 2 ndi 3, chitani chitsanzo chosonyeza njira zolalikirira zomwe zatchulidwa mu ndimezo. Pambuyo pokambirana ndime 4, chitani chitsanzo chosonyeza mmene tingayambitsire phunziro la Baibulo la panyumba pa ulendo wobwereza.
[Mawu a M’munsi]
a Mungasankhe kukambirana bokosi kapena ayi.