Ndandanda ya Mlungu wa October 11
MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 11
□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:
lv mutu 13 ndime 5-14, ndi bokosi patsamba 150a
□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:
Kuwerenga Baibulo: 1 Mbiri 5-7
Na. 1: 1 Mbiri 6:31-47
Na. 2: Kodi Mboni za Yehova Ndi Kagulu Kampatuko, Nanga Chipembedzo Chawo Chakhalapo kwa Utali Wotani? (rs tsa. 273 ndime 4–tsa. 274 ndime 4)
Na. 3: Kodi Zingatheke Bwanji Kuti Anthu Opanda Ungwiro Akhale Oyera? (1 Pet. 1:16)
□ Msonkhano wa Utumiki:
Mph. 5: Zilengezo.
Mph. 10: Kodi Muyenera Kuyankha Bwanji? Nkhani yokambirana ndi omvera yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 69, ndime 1-5. Khalani ndi chitsanzo chosonyeza mpainiya akuyankha munthu amene amaphunzira naye Baibulo yemwe akufunika kupanga chosankha. Wophunzirayo akufunsa kuti: “Kodi mukanakhala inuyo mukanatani pamenepa?”
Mph. 10: Kukhala Waukhondo Kumalemekeza Mulungu. Nkhani yochokera m’buku la Gulu, tsamba 137, ndime 1, mpaka tsamba 138, ndime 2. Pemphani omvera kuti afotokoze mmene ukhondo ndiponso kuoneka bwino kwa Mboni za Yehova kunawathandizira kuphunzira choonadi.
Mph. 10: “Musachite Mantha.” Nkhani ya mafunso ndi mayankho.
[Mawu a M’munsi]
a Mungasankhe kukambirana bokosi kapena ayi.