Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 6/10 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa June 21

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa June 21
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 21
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 6/10 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa June 21

MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 21

Nyimbo Na. 52

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 8 ndime 11-18

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Mafumu 1-2

Na. 1: 1 Mafumu 1:1-14

Na. 2: Kodi Kugwiritsa Ntchito Zifaniziro Polambira Kungakhudze Bwanji Tsogolo Lathu? (rs tsa. 438 ndime 3-6)

Na. 3: N’chifukwa Chiyani Kumvera Mulungu Kumapindulitsa Mwakuthupi Ndiponso Mwauzimu?

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 1

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 15: Mabuku Ogawira mu July. Kukambirana ndi omvera. Fotokozani mwachidule zimene zili m’mabukuwo, ndipo chitani chitsanzo chimodzi kapena ziwiri.

Mph. 15: “Nthawi Zonse Khalani Wokonzeka Kuyambitsa Phunziro la Baibulo.” Kukambirana mwa mafunso ndi mayankho. Chitani chitsanzo chosonyeza mmene tingagwiritsire ntchito kapepala ka Kudziwa Choonadi poyambitsa phunziro la Baibulo pa ulendo wobwereza kwa munthu amene munamupatsa buku limene ligawiridwe mu July.

Nyimbo Na. 47

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena