Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 6/10 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa June 14

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa June 14
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 14
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 6/10 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa June 14

MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 14

Nyimbo Na. 48

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 8 ndime 1-10

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Samueli 22-24

Na. 1: 2 Samueli 22:1-20

Na. 2: Kodi Chilamulo Chinakhala Motani Namkungwi Wotsogolera kwa Khristu? (Agal. 3:24)

Na. 3: Kodi Tiyenera Kuona Bwanji Chifaniziro Chilichonse Chimene Tinkalambira M’mbuyomu? (rs tsa. 437 ndime 5–tsa. 438 ndime 2)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 10

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Kodi Tinachita Zotani pa Nyengo ya Chikumbutso? Nkhani yokambirana ndi omvera. Yamikirani mpingo chifukwa cha zimene unachita mu utumiki pa nyengo ya Chikumbutso, ndipo tchulani zimene zachitika chifukwa cha ntchitoyi. Pemphani omvera kufotokoza zimene anakumana nazo pamene amachita upainiya wothandiza.

Mph. 10: Mphunzitsi Wabwino Amathandiza Wophunzira Wake Kugwiritsira Ntchito Zimene Akuphunzira. Nkhani yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 60.

Mph. 10: “Kodi Diso Lanu Limalunjika Pachinthu Chimodzi?” Nkhani ya mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 7

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena