Ndandanda ya Mlungu wa January 4
MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 4
□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:
lv-CN mutu 1 ndime 1-9 ndiponso mawu oyamba
□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:
Kuwerenga Baibulo: Yoswa 16–20
Na. 1: Yoswa 17:1-10
Na. 2: Kodi Anthu Opita Kumwamba Akachitako Chiyani? (rs-CN tsa. 210 ndime 1 mpaka 5)
Na. 3: Kodi N’chifukwa Chiyani Munthu ‘Wokaikakaika’ Sasangalatsa Mulungu? (1 Maf. 18:21)
□ Msonkhano wa Utumiki:
Mph. 5: Zilengezo.
Mph. 10: Muzigwiritsa Ntchito Mafunso Kuti Muziphunzitsa Mogwira Mtima. Nkhani yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 239.
Mph. 10: Zosowa za pampingo.
Mph. 10: Muzigwiritsa Ntchito Mabuku Ofotokoza za M’Baibulo mu Utumiki Wanu. Kambiranani ndi omvera ndime zitatu za pamutu wakuti “Kugwiritsa Ntchito Mabuku Ofotokoza za M’Baibulo,” tsamba 100 ndi 101 m’buku la Gulu. Pemphani woyang’anira utumiki kapena mkulu wina kuti afotokoze mmene tingamagwiritsire ntchito mosamala mabuku athu.