Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/09 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 9

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 9
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 9
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 11/09 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa November 9

MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 9

Nyimbo Na. 145

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 29 ndime 1-12

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Deuteronomo 19-22

Na. 1: Deuteronomo 22:1-19

Na. 2: Zimene Tingachite Kuti Tikondweretse Mulungu (lr-CN mutu 40)

Na. 3: Kodi a 144,000 Ndi Ayuda Okha? (rs-CN tsa. 208 ndime 4–tsa. 209 ndime 2)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 11

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Udindo Wathu Pogawira Mabuku ndi Magazini. Nkhani yokambirana ndi omvera kuchokera m’buku la Gulu, patsamba 133, ndime 1 mpaka 3. Tsindikani mfundo yakuti wofalitsa aliyense ali ndi udindo wogwiritsira ntchito zinthu za Ufumu mwanzeru.

Mph. 20: “Kodi Tizichita Ulendo Wobwereza Pakatha Nthawi Yaitali Bwanji?” Nkhani yokambirana mwa mafunso ndi mayankho. Chitani chitsanzo chosonyeza wofalitsa akuchita ulendo wobwereza n’cholinga choyambitsa phunziro la Baibulo.

Nyimbo Na. 214

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena