Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 7/09 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa July 13

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa July 13
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JULY 13
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 7/09 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa July 13

MLUNGU WOYAMBIRA JULY 13

Nyimbo Na. 40

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 22 ndime 9-14

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Levitiko 21-24

Na. 1: Levitiko 22:17-33

Na. 2: Kodi Amene Amachita Zinthu Zoipa Angasinthe? (lr-CN mutu 25)

Na. 3: Kodi Akhristu Oona Amachita Chiyani Kuti Athandize Osauka?

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 224

Mph.5: Zilengezo.

Mph.20: “Kodi Mwakonzekera Phwando Lauzimu?” Ikambidwe ndi mlembi wampingo. Tchulani malo amene mpingo wanu ukachitire msonkhano wachigawo. Kambiranani bokosi lakuti, “Zofunika Kukumbukira pa Msonkhano Wachigawo.”

Mph.10: “Kugulitsa Malonda pa Misonkhano Yathu Yachigawo.” Nkhani ndi kukambirana ndi omvera. Tsindikani kufunika kobweretsa chakudya chamasana chopepuka m’malo mochoka pamalo a msonkhano kupita kukagula chakudya kwa ogulitsa chakudya m’misewu ndi ku malesitilanti apafupi ndi malo a msonkhanowo.

Nyimbo Na. 17

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena