Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 6/09 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa June 8

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa June 8
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 8
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 6/09 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa June 8

MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 8

Nyimbo Na. 14

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 20 ndime 13-21 ndi bokosi la patsamba 207

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Levitiko 1-5

Na. 1: Levitiko 4:1-15

Na. 2: Kodi Tiyenera Kudzitama Tikachita Zabwino? (lr-CN mutu 21)

Na. 3: Kodi Akhristu Ayenera Kugwiritsa Ntchito Bwanji Ulamuliro?

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 20

Mph.5: Zilengezo.

Mph.10: Mbali ya Yesu Yofunika Kwambiri pa Chifuniro cha Mulungu. Nkhani yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, pamutu waung’ono patsamba 276.

Mph.10: Buku Logawira mu June. Chitani chitsanzo chimene chakhala chogwira mtima polalikira anthu a m’gawo lanu. Komanso sonyezani mmene mungagwiritsire ntchito bukulo poyambitsa phunziro la Baibulo.

Mph.10: “Timasonyeza Kuti Timakonda Mulungu mwa Utumiki Wathu.” Kambiranani mwa mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 10

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena