Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 2/09 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa February 9

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa February 9
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 9
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 2/09 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa February 9

MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 9

Nyimbo Na. 118

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 14 ndime 1-12

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Genesis 25-28

Na. 1: Genesis 25:1-18

Na. 2: Mphunzitsi Waluso Anatumikira Anthu Ena (lr-CN mutu 6)

Na. 3: Chifukwa Chake Anthu Sangathetse Mavuto Ngakhale Atayesetsa (rs-CN tsa. 63 ndime 5 mpaka tsa. 64 ndime 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 211

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 8: Kapepala Katsopano Koitanira Anthu ku Misonkhano ya Mpingo. Nkhani yofotokoza zimene zili m’kapepalaka komanso mmene tingakagwiritsire ntchito. Kapepalaka kaziperekedwa kwa anthu onse ochita chidwi ndi uthenga wathu. Chitani chitsanzo cha mmene tingagawirire kapepalaka kunyumba ndi nyumba komanso paulendo wobwereza.

Mph. 10: Zokumana Nazo Poyambitsa Maphunziro a Baibulo. Fotokozani mmene zinayendera mwezi watha pampingo wanu, tsiku limene munasankha kuyambitsa maphunziro a Baibulo apanyumba. Alimbikitseni onse kuti azilowa nawo muutumiki patsiku lapadera limeneli.

Mph. 12: “Ntchito Yapadera Yoitanira Anthu ku Chikumbutso.” Kambiranani mwa mafunso ndi mayankho. Gawirani kapepala kamodzi kwa aliyense pamsonkhanowo ndipo kambiranani zimene zili m’kapepalako. Chitani chitsanzo cha mmene tingagawirire kapepalako.

Nyimbo Na. 87

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena