Ndandanda ya Mlungu wa January 19
MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 19
□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:
cl-CN mutu 13, ndime 1-8
□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:
Kuwerenga Baibulo: Genesis 11-16
Na. 1: Genesis 14:1-16
Na. 2: Amene Anapanga Zinthu Zonse (lr-CN mutu 3)
Na. 3: Kodi Yehova Amatiumba Bwanji? (Yes. 64:8)
□ Msonkhano wa Utumiki:
Mph. 5: Zilengezo za pampingo. Musankhe zilengezo zina mu Utumiki Wathu wa Ufumu uno. Limbikitsani onse kuti akawerenge ndi kubweretsa zofalitsa zonse zimene zasonyezedwa m’nkhani ya mlungu wamawa yakuti “Kodi Mukudziwa Zimene Mungasankhe?”
Mph. 10: Opani Mulungu Woona Ndipo Sungani Malamulo Ake. Nkhani yokambidwa ndi mkulu yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 272 ndi 273, ndime 1. Ikambidwe mwaumoyo.
Mph. 10: Mabuku Ogawira mu February. Fotokozani mwachidule zimene zili m’mabukuwo, ndipo khalani ndi chitsanzo chimodzi kapena ziwiri.
Mph. 10: “Kodi Tiyenera Kukumbukira Chiyani Pogwiritsa Ntchito Mafoni a M’manja ndi Mapeja?” Nkhani yokambidwa ndi mkulu, ndipo gwirizanitsani mfundo za nkhaniyi ndi mpingo wanu.