Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/09 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa January 19

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa January 19
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 19
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 1/09 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa January 19

MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 19

Nyimbo Na. 126

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 13, ndime 1-8

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Genesis 11-16

Na. 1: Genesis 14:1-16

Na. 2: Amene Anapanga Zinthu Zonse (lr-CN mutu 3)

Na. 3: Kodi Yehova Amatiumba Bwanji? (Yes. 64:8)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 90

Mph. 5: Zilengezo za pampingo. Musankhe zilengezo zina mu Utumiki Wathu wa Ufumu uno. Limbikitsani onse kuti akawerenge ndi kubweretsa zofalitsa zonse zimene zasonyezedwa m’nkhani ya mlungu wamawa yakuti “Kodi Mukudziwa Zimene Mungasankhe?”

Mph. 10: Opani Mulungu Woona Ndipo Sungani Malamulo Ake. Nkhani yokambidwa ndi mkulu yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 272 ndi 273, ndime 1. Ikambidwe mwaumoyo.

Mph. 10: Mabuku Ogawira mu February. Fotokozani mwachidule zimene zili m’mabukuwo, ndipo khalani ndi chitsanzo chimodzi kapena ziwiri.

Mph. 10: “Kodi Tiyenera Kukumbukira Chiyani Pogwiritsa Ntchito Mafoni a M’manja ndi Mapeja?” Nkhani yokambidwa ndi mkulu, ndipo gwirizanitsani mfundo za nkhaniyi ndi mpingo wanu.

Nyimbo Na. 133

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena