Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w09 10/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2009
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO:
Nsanja ya Olonda—2009
w09 10/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

October 15, 2009

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

November 30, 2009–December 6, 2009

“Yakani ndi Mzimu”

TSAMBA 3

NYIMBO ZOIMBA: 191, 177

December 7-13, 2009

‘Khalani Mwamtendere ndi Anthu Onse’

TSAMBA 7

NYIMBO ZOIMBA: 159, 206

December 14-20, 2009

‘Ndinu Mabwenzi Anga’

TSAMBA 13

NYIMBO ZOIMBA: 224, 217

December 21-27, 2009

Mungathe Kukhalabe ndi Mabwenzi M’dziko Lopanda Chikondi Lino

TSAMBA 17

NYIMBO ZOIMBA: 173, 155

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

Nkhani Zophunzira 1, 2 MASAMBA 3-11

Nkhani zimenezi zikufotokoza mavesi onse a Aroma chaputala 12, malinga ndi mfundo za m’mavesiwo. Tikambirana zimene mawu akuti “yakani ndi mzimu” amatanthauza ndiponso mmene tingaperekere matupi athu nsembe yamoyo kwa Mulungu. Tiphunziranso mmene tingalimbikitsire mtendere panyumba ndi mumpingo, ndiponso mmene tingagonjetsere choipa mwa kuchita chabwino.

Nkhani Zophunzira 3, 4 MASAMBA 13-21

Kodi kukhala bwenzi labwino kumatanthauza chiyani? Nkhani zimenezi zitithandiza kuona chitsanzo chabwino chimene Yesu anapereka pa nkhani imeneyi. Tionanso zimene Akhristu oyambirira anachita potengera chitsanzo chake. Zifotokozanso chifukwa chake ndi zothandiza masiku ano kukhala pa ubwenzi wabwino ndiponso wolimba, komanso mmene tingachitire zimenezi.

M’MAGAZINI INO MULINSO:

Mafunso Ochokera kwa Owerenga

TSAMBA 12

Mmene Misonkhano Yachigawo Itatu Inasinthira Moyo Wanga

TSAMBA 22

Kodi ‘Mwazika Mizu ndi Kukhazikika pa Maziko’?

TSAMBA 26

Kulambira kwa Pabanja N’kofunika Kwambiri Kuti Tidzapulumuke

TSAMBA 29

Kodi Mwapatula Nthawi Yophunzirira Baibulo?

TSAMBA 32

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena