Zamkatimu
November 15, 2008
Magazini Yophunzira
NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
January 5-11, 2009
Thandizani Osochera Kubwerera M’gulu la Nkhosa
TSAMBA 8
NYIMBO ZOIMBA: 47, 101
January 12-18, 2009
Athandizeni Kubwerera Mwamsanga
TSAMBA 12
NYIMBO ZOIMBA: 116, 184
January 19-25, 2009
Samalirani Thanzi Lanu M’njira Yogwirizana ndi Malemba
TSAMBA 23
NYIMBO ZOIMBA: 44, 182
January 26, 2009–February 1, 2009
“Tsutsani Mdyerekezi” Monga Anachitira Yesu
TSAMBA 27
NYIMBO ZOIMBA: 174, 191
Cholinga cha Nkhani Zophunzira
Nkhani Zophunzira 1, 2 MASAMBA 8-16
M’nkhanizi tiphunzira mmene akulu ndiponso anthu ena mumpingo angathandizire abale ndi alongo amene achoka m’gulu la nkhosa la Mulungu. Nkhani zimenezi zikuthandizani kudziwa zimene mungachite kuti muthandize Akhristu ofooka. Zikuthandizaninso kuyankha funso lakuti, kodi anthu amene akubwerera m’gulu ayenera kuyembekezera kudzalandiridwa motani?
Nkhani Yophunzira 3 MASAMBA 23-27
Mwachibadwa anthufe timaganizira za thanzi lathu. N’chifukwa chake Mboni za Yehova zikadwala zimafuna kulandira chithandizo. Komabe m’pofunika ‘kuganiza bwino.’ (Tito 2:12) Ndipotu chofunika kwambiri ndicho kusamalira thanzi lathu lauzimu ndi kulimbitsa ubwenzi wathu ndi Mulungu.
Nkhani Yophunzira 4 MASAMBA 27-31
Dziwani mmene Yesu Khristu anaperekera chitsanzo potsutsa Mdyerekezi. Nkhani imeneyi ikusonyeza kuti Mulungu amamukhulupirira Mwana wake ndipo ikupereka zifukwa zake. Ikusonyeza zimene zinam’thandiza Yesu kuti atsutse Mdyerekezi ndipo ikufotokoza mmene ifenso tingachitire zimenezi.
M’MAGAZINI INO MULINSO:
Kodi Mumafuna Mutakhala Munthu Wotani?
TSAMBA 3
Kutumikira Mulungu ndi “Mtima Umodzi ndi Maganizo Amodzi”
TSAMBA 6
“Titsatire Zinthu Zodzetsa Mtendere”
TSAMBA 17
Mawu a Yehova Ndi Amoyo—Mfundo Zazikulu za M’makalata a Yakobe ndi Petulo
TSAMBA 20
Mpukutu Wotchedwa “Nyimbo ya Panyanja” Umatithandiza Kudziwa Zinthu Zakale
TSAMBA 32