Tsamba 2
Miliri—Kodi Idzathadi? 3-10
Ngakhale pali kupita patsogolo m’zamankhwala ndi zasayansi, miliri ndi matenda ena zikuwonjezekabe. Kodi miliri m’zaka za zana la 20 zino imakwaniritsa maulosi a m’Baibulo a masiku otsiriza? Kodi tidzakhalapo ndi dziko lopanda matenda?
Njira Zisanu ndi Imodzi Zotetezera Thanzi Lanu 11
Ŵerengani za njira zisanu ndi imodzi zomwe mungatsate kudzitetezera nokha ndi banja lanu ku tizilombo toyambitsa matenda tomwe tingawononge thanzi lanu.
Kodi Akristu Ayenera Kuda Ochita Mathanyula? 13
Lingaliro la Baibulo Nlotani?