Tsamba 2
Nchifukwa Ninji Pali Chidani Chochuluka? Nchifukwa Ninji Pali Chikondi Chochepa? 3-11
Moyo ungakhale wosangalatsa kwambiri pamene tikukhala ndi anthu omwe timakonda! Koma chikondi chikusoŵeka kwambiri m’dziko lamakono. Kodi nchifukwa ninji chidani chili chofala? Kodi zimenezi zidzasinthadi?
Mboni za Yehova ku Russia 14
Ŵerengani mmene katswiri wa zaumulungu wa ku Russia anaongolerera malingaliro angapo olakwa ponena za Mboni za Yehova.
[Chithunzi patsamba 2]
Tina Gerson/Los Angeles Daily News