Tsamba 2
Munda wa Maluŵa wa Dziko Lonse—Kodi Ndi Maloto Kapena Udzakhalakodi Mtsogolo? 3-10
Anthu amakonda minda ya maluŵa yabata yokhala ndi zomera, mitsinje, ndi matamanda a madzi. Ŵerengani mmene dziko lonse lapansi lidzakhalira munda wa maluŵa wokongola.
Kodi Nkotheka Kupulumutsa Ukwati Mnzanu Atachimwa? 24
Pamene wina wachimwa muukwati, kodi ukwatiwo uyenera kutha?
Kugulitsa Ana mu Uhule—Vuto la Dziko Lonse 27
Wotchedwa kuti “upandu waunyama koposa ndi wonyansitsa.” Kodi nchiyani chidzauthetsa?
[Mawu a Chithunzi patsamba 2]
Chithandizo pa Maphunziro a Kakhalidwe 32