Tsamba 2
Upandu Wolinganiza Mmene Umakukhudzirani 3-10
Upandu wapadziko lonse umakhudza aliyense. Zinthu zonse zakwera mtengo—kuyambira kutaya zinyalala mpaka majuwelo, zovala mpaka simenti. Apandu amaopseza ndi kupseteka oweruza, apolisi, ndi andale. Kodi pali njira youthetsera?
Choonadi Ponena za Bodza 17
Monga momwe chotengera chadothi chingaphwanyikire chitagwetsedwa, unansi wamtengo wapatali nawonso ungawonongeke ndi bodza. Kodi ndi choonadi chanji ponena za bodza chimene tiyenera kudziŵa?
Kodi Ana Ayenera Kudzisankhira Chipembedzo Chawo? 20
Makolo ena amanena kuti ana sayenera kuphunzitsidwa chipembedzo koma kuti ayenera kudzisankhira okha atakula. Kodi Baibulo limanenanji?
[Mawu a Chithunzi patsamba 2]
Mapu: Mountain High Maps® Copyright © 1995 Digital Wisdom, Inc.
[Mawu a Chithunzi patsamba 2]
The Doré Bible Illustrations/Dover Publications, Inc.