Tsamba 2
Isitala—Kodi Imatanthauzanji kwa Inuyo? 3-9
Isitala yanenedwa kukhala phwando lachipembedzo lalikulu la Chikristu Chadziko. Anthu ambiri amaiwona kukhala maziko a chikhulupiriro cha Chikristu. Kodi inuyo mumailingalira motani Isitala? Chofunika koposa, kodi imatanthauzanji kwa Mulungu?
Kodi Nchifukwa Ninji Ndiyenera Kuika Nzeru Kumaphunziro Pasukulu? 23
Achichepere amafuna kudziŵa chifukwa chake ayenera kuyesayesa mwamphamvu pasukulu pamene ena ambiri samatero
“Ndinalira ndi Chimwemwe” 26
Oŵerenga Galamukani! kumbali zonse zadziko amasonyeza chiyamikiro chawo chachikulu cha mpambo wa “Kupoletsa Mabala a Kuchitira Nkhanza Ana”