LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
Baibo ya Cimasulilo ca Dziko Latsopano

Za m’Buku la 2 Timoteyo

2 TIMOTEYO

ZA M’BUKULI

  • 1

    • Mau oyamba (1, 2)

    • Paulo ayamika Mulungu cifukwa ca cikhulupililo ca Timoteyo (3-5)

    • Kukolezela mphatso ya Mulungu ngati moto (6-11)

    • Kugwilitsitsa mau olondola (12-14)

    • Adani komanso mabwenzi a Paulo (15-18)

  • 2

    • Kuphunzitsa oyenelela kukhala aphunzitsi (1-7)

    • Kupilila mabvuto cifukwa ca uthenga wabwino (8-13)

    • Kufotokoza bwino mau a uthenga wabwino (14-19)

    • Kuthawa zilakolako za unyamata (20-22)

    • Mocitila ndi otsutsa (23-26)

  • 3

    • Masiku otsiliza adzakhala nthawi yobvuta (1-7)

    • Kutengela citsanzo ca Paulo mosamala (8-13)

    • “Pitiliza kutsatila zimene unaphunzila” (14-17)

      • Malemba onse anauzilidwa ndi Mulungu (16)

  • 4

    • “Uzikwanilitsa mbali zonse za utumiki wako” (1-5)

      • Lalikila mau modzipeleka (2)

    • “Ndamenya nkhondo yabwino” (6-8)

    • Zina zimene Paulo anakamba (9-18)

    • Kupeleka moni (19-22)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2026)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani