LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
Baibo ya Cimasulilo ca Dziko Latsopano

Za m’Buku la 1 Timoteyo

1 TIMOTEYO

ZA M’BUKULI

  • 1

    • Mau oyamba (1, 2)

    • Cenjezo lokhudza aphunzitsi abodza (3-11)

    • Cisomo cimene Paulo anacitilidwa (12-16)

    • Mfumu yamuyaya (17)

    • “Kumenya nkhondo yabwino” (18-20)

  • 2

    • Kupemphelela anthu osiyana-siyana (1-7)

      • Mulungu mmodzi komanso mkhalapakati mmodzi (5)

      • Dipo la anthu onse lokwanila ndendende (6)

    • Malangizo kwa amuna ndi akazi (8-15)

      • Kubvala mwaulemu (9, 10)

  • 3

    • Ziyenelezo kuti munthu akhale woyang’anila (1-7)

    • Ziyenelezo za atumiki othandiza (8-13)

    • Cinsinsi copatulika ca kudzipeleka kwa Mulungu (14-16)

  • 4

    • Cenjezo lokhudza ziphunzitso za ziwanda (1-5)

    • Mmene munthu angakhalile mtumiki wabwino wa Khristu (6-10)

      • Masewela olimbitsa thupi komanso kudzipeleka kwa Mulungu (8)

    • Uzisamala ndi zimene umaphunzitsa (11-16)

  • 5

    • Mocitila ndi acikulile komanso acinyamata (1, 2)

    • Thandizo kwa akazi amasiye (3-16)

      • Kusamalila banja (8)

    • Kucitila ulemu akulu ogwila nchito mwakhama (17-25)

      • “Uzimwako vinyo pang’ono, cifukwa ca bvuto lako la m’mimba” (23)

  • 6

    • Akapolo azilemekeza ambuye ao (1, 2)

    • Aphunzitsi onyenga komanso anthu okonda ndalama (3-10)

    • Malangizo kwa munthu wa Mulungu (11-16)

    • Kulemela pa nchito zabwino (17-19)

    • Teteza zimene unalandila (20, 21)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2026)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani