LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
Baibo ya Cimasulilo ca Dziko Latsopano

Za m’Buku la Aefeso

AEFESO

ZA M’BUKULI

  • 1

    • Moni (1, 2)

    • Madalitso auzimu (3-7)

    • Kusonkhanitsa zinthu zonse kwa Khristu (8-14)

      • “Dongosolo” pa nthawi yoikidwilatu (10)

      • Kuikidwa cidindo ndi mzimu woyela monga cikole cotsimikizila (13, 14)

    • Paulo anathokoza Mulungu kaamba ka cikhulupililo ca Aefeso ndipo anawapemphelela (15-23)

  • 2

    • Anapangitsa kuti akhale amoyo mogwilizana ndi Khristu (1-10)

    • Anagwetsa cipupa cimene cinali kuwalekanitsa (11-22)

  • 3

    • Cinsinsi copatulika cinaphatikizapo anthu a mitundu ina (1-13)

      • Anthu a mitundu ina adzalamulila pamodzi ndi Khristu (6)

      • Colinga camuyaya ca Mulungu (11)

    • Apemphelela Aefeso kuti akhale ozindikila (14-21)

  • 4

    • Mgwilizano m’thupi la Khristu (1-16)

      • Mphatso za amuna (8)

    • Umunthu wakale komanso watsopano (17-32)

  • 5

    • Malankhulidwe abwino komanso khalidwe loyela (1-5)

    • Muziyenda ngati ana akuwala (6-14)

    • Dzadzidwani ndi mzimu (15-20)

      • Muziigwilitsa nchito bwino nthawi yanu (16)

    • Malangizo kwa amuna ndi akazi okwatila (21-33)

  • 6

    • Malangizo kwa ana ndi makolo (1-4)

    • Malangizo kwa akapolo ndi ambuye (5-9)

    • Bvalani zida zonse zankhondo zocokela kwa Mulungu (10-20)

    • Moni womaliza (21-24)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2026)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani