Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Loyamba Mkati Mwachikuto Mutu wa Kabuku Kano/Tsamba la Ofalitsa Zamkatimu Mawu Oyamba Zomwe Zili M’bukuli GAWO 1 Kukhala Ndi Makolo Komanso Achibale Kodi Ndingatani Kuti Ndizilankhula Momasuka ndi Makolo Anga? N’chifukwa Chiyani Ndimangokhalira Kukangana ndi Makolo Anga? Kodi Ndingatani Kuti Makolo Anga Azindilolako Kuchita Zinthu Zina? N’chifukwa Chiyani Banja la Makolo Anga Linatha? Kodi Ndingatani Ngati Makolo Anga Akwatiranso? Kodi Ndingatani Kuti Ndizigwirizana Ndi Abale Anga? Chitsanzo Chabwino—Yakobo Kodi Ndine Wokonzeka Kusamuka N’kumakakhala Ndekha? Mfundo zanga—Kukhala Ndi Makolo Komanso Achibale GAWO 2 Khalidwe Lanu Kodi Ndingapeze Bwanji Anzanga Abwino? Kodi Ndingatani Kuti Ndisamakopeke Ndi Zochita za Anzanga? N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kusamalira Thanzi Langa? Kodi Ndizivala Bwanji? Kodi Ndingatani Kuti Ndisamadziderere? Kodi Ndingatani Kuti Ndisamangokhala Wokhumudwa? Chitsanzo Chabwino—Yobu Bwanji Ndingodzipha? Kodi N’kulakwa Kufuna Kuchitako Zinthu Zina Pandekha? N’chiyani Chingandithandize Kupirira Ngati Mayi Kapena Bambo Anga Anamwalira? Mfundo Zanga—Khalidwe Lanu GAWO 3 Zochitika Kusukulu N’chifukwa Chiyani Ndimaopa Kuuza Anzanga Akusukulu Zimene Ndimakhu Lupirira? Kodi Ndingatani Ngati Ndimapanikizika Kwambiri Kusukulu? Bwanji Ndingosiya Sukulu? Kodi Ndingatani Kuti Ndizigwirizana Ndi Aphunzitsi Anga? Chitsanzo Chabwino—Mose Kodi Ndingatani Kuti Ndizigwiritsa Ntchito Nthawi Yanga Mwanzeru? Kodi Nditsatire Chikhalidwe Chiti? Mfundo Zanga—Zochitika Kusukulu GAWO 4 Kugonana, Makhalidwe ndi Chikondi Kodi Ndingafotokoze Bwanji Zimene Baibulo Limanena pa Nkhani Yogonana Amuna Kapena Akazi Okhaokha? Kodi Kugonana Tili Pachibwenzi Kungachititse Kuti Tizikondana Kwambiri? Kodi Ndingatani Kuti Ndisiye Chizolowezi Choseweretsa Maliseche? Kodi Kugonana Pongofuna Kuthandizana Kuli Ndi Vuto? N’chifukwa Chiyani Anyamata Samandifunsira? N’chifukwa Chiyani Atsikana Samandifuna? Kodi Ndingadziwe Bwanji Ngati Chilidi Chikondi Chenicheni? Kodi Ndife Okonzekadi Kulowa M’banja? Chitsanzo Chabwino—Rute Kodi Ndingatani Ngati Chibwenzi Chatha? Kodi Ndingadziteteze Bwanji Kwa Anthu Ogwiririra Anzawo? Mfundo Zanga—Kugonana, Makhalidwe ndi Chikondi GAWO 5 Makhalidwe Amene Angawononge Moyo Wanu Kodi Mumadziwa Zotani pa Nkhani ya Fodya? Kodi Kumwa Mowa Wambiri Kuli Ndi Vuto Lanji? Kodi Ndingatani Kuti Ndisiye Kugwiritsa Ntchito Mankhwala Osokoneza Bongo? Mfundo Zanga—Makhalidwe Amene Angawononge Moyo Wanu GAWO 6 Zimene Mumachita Pa Nthawi Yopuma Kodi Ndimagwiritsa Ntchito Zipangizo Zamakono Mopitirira Muyezo? N’chifukwa Chiyani Makolo Anga Samandilola Kuti Ndizisangalalako Nthawi Zina? Mfundo Zanga—Zimene Mumachita pa Nthawi Yopuma GAWO 7 Kulambira Mulungu Kodi Ndingatani Kuti Kulambira Mulungu Kuzindisangalatsa? Kodi Ndingatani Kuti Ndikwaniritse Zolinga Zanga? Chitsanzo Chabwino—Timoteyo Mfundo Zanga—Kulambira Mulungu Zakumapeto Zimene Munalemba Zokuthandizani Kupeza Mkati Mwachikuto Kumapeto Chikuto Chakumbuyo