Mawu a M'munsi
b MAWU OFOTOKOZERA ZITHUNZI: Chithunzi chilichonse chikusonyeza bambo ali ndi mwana wake: (1) Akumvetsera zimene mwana akunena. (2) Akupezera mwana wake zinthu zofunika. (3) Akuphunzitsa mwana wake. (4) Akutonthoza mwana wake. Chithunzi cha dzanja la Yehova chimene chikuonekacho chikusonyeza kuti Yehova amatisamaliranso chimodzimodzi.