Mawu a M'munsi
a Nthawi zambiri tikaganizira za Yehova timaona kuti ndi Mlengi wathu komanso Wolamulira Wamkulu. Koma palinso zifukwa zotichititsa kumuona kuti ndi Atate wathu wachikondi. Munkhaniyi tikambirana zifukwazo. Tikambirananso zifukwa zotitsimikizira kuti Yehova sadzatisiya.