Mawu a M'munsi
a Anthu ambiri amadziwa kuti Mulungu aliko koma samudziwa bwino. Kodi kudziwa Yehova kumatanthauza chiyani? Nanga tingaphunzire chiyani kwa Mose ndi Mfumu Davide pa nkhani yolimbitsa ubwenzi wathu ndi Mulungu? Munkhaniyi tikambirana mayankho a mafunso amenewa.