Mawu a M'munsi
h MAWU OFOTOKOZERA ZITHUNZI: Mu February 2019, M’bale Gerrit Lösch wa m’Bungwe Lolamulira anatulutsa Baibulo la Dziko Latsopano lokonzedwanso m’Chijeremani ndipo anthu anasangalala kwambiri. Masiku ano, ofalitsa ambiri, ngati alongo awiriwa, amasangalala kuligwiritsa ntchito mu utumiki.