Mawu a M'munsi
b Timoteyo analoleranso kuti adulidwe ngakhale kuti pa nthawiyo Akhristu sankafunikanso kudulidwa. Paulo ndi amene analamula zimenezi chifukwa choti Ayuda ankadziwa kuti bambo a Timoteyo anali Mgiriki. Anachita zimenezi kuti Ayudawo asamupezere zifukwa.—Machitidwe 16:3.