Mawu a M'munsi
c Zimenezi zingamveke ngati zodabwitsa, koma sizinali zachilendo m’nthawi imeneyo. Katswiri wina wachigiriki wolemba mbiri yakale, dzina lake Herodito, anafotokoza kuti panthawi ina Aperisi analira maliro a kazembe wina wake wotchuka, ndipo anachita mwambo wa malirowo limodzi ndi ziweto zawo zomwe.