Mawu a M'munsi
a The New English Bible limati pa Salmo 96:1: “Imbirani AMBUYE, anthu onse a padziko lapansi!” The Contemporary English Version limati: “Aliyense padziko lapansi, aimbe zitamando kwa AMBUYE.” Zimenezi zikugwirizana ndi mfundo yakuti Yesaya potchula “dziko lapansi latsopano” anali kutanthauza anthu a Mulungu m’dziko lakwawo.