Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Kumeneku kunali kuphonya kumene mipingo yambiri ya Dziko Lachikristu inachita. Lutheran linali dzina lowajeda nalo limene adani a Martin Luther anapatsa otsatira ake, amenenso analilandira. Mofananamo, a Baptist analandira dzina lowajeda nalo limene akunja anawapatsa chifukwa chakuti iwo ankalalikira ubatizo wa kumiza. Mofanananso ndi zimenezo, zichita ngati kuti a Methodist analandira dzina limene akunja anawapatsa. Ponena za mmene a Society of Friends anafikira pa kutchedwa Quakers, The World Book Encyclopedia imati: “Liwulo Quaker poyamba linali lotonza Fox [myambitsi wake], amene anauza woweruza Wachingelezi ‘kunthunthumira ndi Mawu a Ambuye.’ Woweruzayo anatcha Fox ‘quaker.’”

Mabuku a Chichewa (1974-2026)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena