Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

e Ambiri amaona kusintha m’cholembedwa cha Luka pambuyo pa Luka 21:24. Dr. Leon Morris akuti: “Yesu ayamba kulankhula za nthaŵi za Akunja. . . . Malinga ndi kunena kwa akatswiri ochuluka chisamaliro tsopano chikuikidwa pakudza kwa Mwana wa munthu.” Profesa R. Ginns akulemba kuti: “Kudza kwa Mwana wa Munthu​—(Mt 24:29-31; Mr 13:24-27). Kutchulidwa kwa ‘nthaŵi za Akunja’ kumapereka mawu oyamba a mutu umenewu; malingaliro [a Luka] tsopano akupyola pachiwonongeko cha Yerusalemu ndi kupita mtsogolo.”

Mabuku a Chichewa (1974-2026)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2026 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena