Mawu a M'munsi
e Ambiri amaona kusintha m’cholembedwa cha Luka pambuyo pa Luka 21:24. Dr. Leon Morris akuti: “Yesu ayamba kulankhula za nthaŵi za Akunja. . . . Malinga ndi kunena kwa akatswiri ochuluka chisamaliro tsopano chikuikidwa pakudza kwa Mwana wa munthu.” Profesa R. Ginns akulemba kuti: “Kudza kwa Mwana wa Munthu—(Mt 24:29-31; Mr 13:24-27). Kutchulidwa kwa ‘nthaŵi za Akunja’ kumapereka mawu oyamba a mutu umenewu; malingaliro [a Luka] tsopano akupyola pachiwonongeko cha Yerusalemu ndi kupita mtsogolo.”